Yeremiya 32:37 BL92

37 Taonani, ndidzawasokolotsa m'maiko monse, kumene ndinawapitikitsira ndi mkwiyo wanga, ndi m'kupsa mtima kwanga, ndi mu ukali waukuru, ndipo ndidzawabwezeranso kumalo kuno, ndipo ndidzawakhazikitsa mokhulupirika,

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 32

Onani Yeremiya 32:37 nkhani