Yeremiya 35:14 BL92

14 Mau a Yonadabu mwana wa Rekabu, amene anauza ana ace, asamwe vinyo, alikucitidwa, ndipo mpaka lero samamwa, pakuti amvera lamulo la kholo lao; koma Ine ndanena ndi inu, ndalawirira ndi kunena; koma simunandimvera Ine.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 35

Onani Yeremiya 35:14 nkhani