Yeremiya 36:29 BL92

29 Ndipo za Yehoyakimu mfumu ya Yuda uziti, Yehova atero: Iwe watentha mpukutu uwu, ndi kuti, Bwanji walemba m'menemo, kuti, Mfumu ya ku Babulo idzadzadi nidzaononga dziko ili, nidzatha m'menemo anthu ndi nvama?

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 36

Onani Yeremiya 36:29 nkhani