Yeremiya 36:6 BL92

6 koma pita iwe, nuwerenge mu mpukutu umene ndakulembetsa, mau a Yehova m'makutu a anthu m'nyumba ya Yehova tsiku lakusala kudya; ndiponso udzawawerenga m'makutu a Ayuda onse amene aturuka m'midzi yao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 36

Onani Yeremiya 36:6 nkhani