Yeremiya 39:5 BL92

5 Koma nkhondo ya Akasidi inawalondola, nimpeza Zedekiya m'zidikha za Yeriko; ndipo atamgwira, anamtengera kwa Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo ku Ribila m'dziko la Hamati, ndipo iye ananena naye mlandu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 39

Onani Yeremiya 39:5 nkhani