Yeremiya 39:4 BL92

4 Ndipo panali pamene Zedekiya mfumu ya Yuda ndi amuna onse a nkhondo anawaona, anathawa naturuka m'mudzi usiku, panjira pa munda wa mfumu, pa cipata ca pakati pa makoma awiri; ndipo iye anaturukira pa njira ya kucidikha.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 39

Onani Yeremiya 39:4 nkhani