Yeremiya 50:11 BL92

11 Cifukwa mukondwa, cifukwa musekerera, inu amene mulanda colowa canga, cifukwa muli onenepa monga ng'ombe yamsoti yoponda tirigu, ndi kulira ngati akavalo olimba;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 50

Onani Yeremiya 50:11 nkhani