Yeremiya 7:20 BL92

20 Cifukwa cace, ati Ambuye Mulungu, Taonani, mkwiyo wanga ndi ukali wanga udzathiridwa pa malo ano, pa anthu, ndi pa nyama, ndi pa mitengo ya m'munda, ndi pa zipatso zapansi; ndipo udzatentha osazima.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 7

Onani Yeremiya 7:20 nkhani