Yeremiya 22:23 BL92

23 Iwe wokhala m'Lebano, womanga cisa cako m'mikungudza, udzacitidwa cisoni cacikuru nanga pamene mapweteko adzadza kwa iwe, monga mkazi alinkudwala!

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 22

Onani Yeremiya 22:23 nkhani