Yeremiya 25:29 BL92

29 Pakuti, taonani, ndiyamba kucita coipa pa mudzi umene uchedwa ndi dzina langa, kodi inu mudzakhala osalangidwa konse? Simudzakhala osalangidwa; pakuti ndidzaitana lupanga ligwe pa onse okhala m'dziko lapansi, ati Yehova wa makamu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:29 nkhani