Yeremiya 25:30 BL92

30 Cifukwa cace muwanenere iwo mau onse awa, ndi kuti kwa iwo, Yehova adzabangula kumwamba, nadzachula mau ace mokhalamo mwace moyera; adzabangulitsira khola lace; adzapfuula, monga iwo akuponda mphesa, adzapfuulira onse okhala m'dziko lapansi.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:30 nkhani