Yeremiya 31:8 BL92

8 Taonani, ndidzatenga iwo ku dziko la kumpoto, ndidzasonkhanitsa iwo ku malekezero a dziko lapansi, pamodzi ndi osaona ndi opunduka mwendo, mkazi amene ali ndi pakati ndi mkazi alinkubala pamodzi; khamu lalikuru lidzabwera kuno.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 31

Onani Yeremiya 31:8 nkhani