Yeremiya 50:34 BL92

34 Mombolo wao ngwa mphamvu; dzina lace Yehova wa makamu: adzawanenera mlandu wao ndithu; kuti apumitse dziko lapansi, nadzidzimutse okhala m'Babulo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 50

Onani Yeremiya 50:34 nkhani