Yesaya 10:24 BL92

24 Cifukwa cace atero Ambuye; Yehova wa makamu, Inu anthu anga okhala m'Ziyoni, musaope Asuri; ngakhale amenya inu ndi cibonga, kapena kukusamulira iwe ndodo yace, monga amacitira Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 10

Onani Yesaya 10:24 nkhani