3 Ndipo mzimu wa Aigupto adzakhala wacabe pakati pace; ndipo Ine ndidzaononga uphungu wace; ndimo iwo adzafunafuna mafano ndi anyanga, ndi alauli, ndi obwebweta.
Werengani mutu wathunthu Yesaya 19
Onani Yesaya 19:3 nkhani