Yesaya 21:2 BL92

2 Masomphenya obvuta aonetsedwa kwa ine; wogula malonda wonyenga amangonyenga, ndi wofunkha amangofunkha. Kwera Elamu iwe; zunguniza Media iwe; kuusa moyo kwace konse ndakutonthoza.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 21

Onani Yesaya 21:2 nkhani