Yesaya 26:19 BL92

19 Akufa anu adzakhala ndi moyo; mitembo yao idzauka. Ukani muyimbe, inu amene mukhala m'pfumbi; cifukwa mame ako akunga mame a pamasamba, ndipo dziko lapansi lidzaturutsa mizimu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 26

Onani Yesaya 26:19 nkhani