Yesaya 27:1 BL92

1 Tsiku limenelo Yehova ndi lupanga lace lolimba ndi lalikuru ndi lamphamvu adzalanga nangumi njoka yotamanga, ndi nangumi njoka yopindika-pindika; nadzapha cing'ona cimene ciri m'nyanja.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 27

Onani Yesaya 27:1 nkhani