Yesaya 28:7 BL92

7 Koma iwonso adzandima ndi vinyo, nasocera ndi cakumwa caukali, wansembe ndi mneneri adzandima ndi cakumwa caukali, iwo amezedwa ndi vinyo, nasocera ndi cakumwa caukali, adzandima popenya, napunthwa poweruza.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 28

Onani Yesaya 28:7 nkhani