Yesaya 33:1 BL92

1 Tsoka kwa iwe amene usakaza, cinkana sunasakazidwa; nupangira ciwembu, cinkana sanakupangira iwe ciwembu! Utatha kusakaza, iwe udzasakazidwa; ndipo utatha kupangira ciwembu, iwo adzakupangira iwe ciwembu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 33

Onani Yesaya 33:1 nkhani