Yesaya 36:22 BL92

22 Ndipo anafika Eliakimu, mwana wa Hilikiya, amene anali wapanyumba, ndi Sebina, mlembi, ndi Yoaki, mwana wa Asafu, mkumbutsi, kwa Hezekiya ndi zobvala zao zong'ambika, namuuza iye mau a kazembeyo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 36

Onani Yesaya 36:22 nkhani