9 Bwanji tsono iwe ungathe kubweza nkhope ya nduna mmodzi wamng'ono wa atumiki a mbuyanga, ndi kukhulupirira Aigupto, kuti adzakupatsa magareta ndi apakavalo?
Werengani mutu wathunthu Yesaya 36
Onani Yesaya 36:9 nkhani