Yesaya 38:1 BL92

1 Masiku amenewo Hezekiya anadwala, nafuna kufa. Ndipo Yesaya mneneri, mwana wa Amozi, anadza kwa iye, nati kwa iye, Atero Yehova, Konza nyumba yako, pakuti iwe udzafa, sudzakhala ndi moyo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 38

Onani Yesaya 38:1 nkhani