Yesaya 39:8 BL92

8 Ndipo Hezekiya anati kwa Yesaya, Mau a Yehova, amene iwe wanena, ali abwino. Iye anatinso, Pakuti padzakhala mtendere ndi zoonadi masiku anga.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 39

Onani Yesaya 39:8 nkhani