2 Tsiku limenelo mphukira ya Yehova idzakhala yokongola ndi ya ulemerero, cipatso ca nthaka cidzakhala cokometsetsa ndi cokongola, kwa iwo amene adzapulumuka a Israyeli.
Werengani mutu wathunthu Yesaya 4
Onani Yesaya 4:2 nkhani