Yesaya 4:5 BL92

5 Ndipo Yehova adzalenga pokhala ponse pa phiri la Ziyoni, ndi pa masonkhano ace, mtambo ndi utsi usana, ndi kung'azimira kwa malawi a moto usiku; cifukwa kuti pa ulemerero wonse padzayalidwa cophimba.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 4

Onani Yesaya 4:5 nkhani