Yesaya 40:24 BL92

24 Inde sanaokedwe, inde sanafesedwe; inde, muzu wao sunazike pansi; koma Iye anawaombetsera mphepo, ndipo afota, ndipo kabvumvulu awacotsa monga ciputu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 40

Onani Yesaya 40:24 nkhani