Yesaya 41:25 BL92

25 Ndautsa wina wakucokera kumpoto; ndipo iye wafika wakucokera poturuka dzuwa, amene achula dzina langa; ndipo iye adzafika pa olamulira, monga matope, ndi monga muumbi aponda dothi la mbiya.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 41

Onani Yesaya 41:25 nkhani