Yesaya 44:13 BL92

13 Mmisiri wa mitengo atambalitsa cingwe; nalilemba ndi colembera, nalikonza ndi ncerero, nalilemba ndi zolinganizira, nalifanizira monga maonekedwe a munthu, monga munthu wokongola, kuti likhale m'nyumba.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 44

Onani Yesaya 44:13 nkhani