Yesaya 45:8 BL92

8 Igwani pansi, inu m'mwamba, kucokera kumwamba, thambo litsanulire pansi cilungamo; dziko lapansi litseguke, kuti libalitse cipulumutso, nilimeretse cilungamo cimere pamodzi; Ine Yehova ndinacilenga cimeneco.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 45

Onani Yesaya 45:8 nkhani