Yesaya 50:4 BL92

4 Ambuye Yehova wandipatsa Ine lilime la ophunzira, kuti ndidziwe kunena mau akucirikiza iye amene ali wolema. Iye andigalamutsa m'mawa ndi im'mawa, nagalamutsa khutu langa kuti limve monga ophunzira.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 50

Onani Yesaya 50:4 nkhani