Yesaya 55:5 BL92

5 Taona, iwe udzaitana mtundu umene sunaudziwa, ndi mtundu umene sunakudziwa udzakuthamangira, cifukwa ca Yehova Mulungu wako, ndi cifukwa ca Woyera wa Israyeli; pakuti Iye wakukometsa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 55

Onani Yesaya 55:5 nkhani