Yesaya 64:6 BL92

6 Pakuti ife tonse takhala ngati wina amene ali wosakonzeka; ndi zolungama zathu zonse ziri ngati cobvala codetsedwa; ndipo ife tonse tifota monga tsamba, ndi zoipa zathu zitiuluza monga mphepo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 64

Onani Yesaya 64:6 nkhani