Yesaya 65:1 BL92

1 Iwo amene sanafunsa za Ine andifunafuna; ndi iwo amene sanandipwaira andipeza; ndinati, Taonani Ine, taonani Ine, kwa mtundu umene sunachula dzina langa.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 65

Onani Yesaya 65:1 nkhani