Yesaya 66:1 BL92

1 Atero Yehova, Kumwamba ndi mpando wanga wacifumu, ndi dziko lapansi ndi coikapo mapazi anga; mudzandimangira Ine nyumba yotani? ndi malo ondiyenera kupumamo ali kuti?

Werengani mutu wathunthu Yesaya 66

Onani Yesaya 66:1 nkhani