Yesaya 7:3 BL92

3 Ndipo Yehova anati kwa Yesaya, Turuka tsopano kukacingamira Ahazi, iwe ndi Seariyasubu, mwana wamwamuna wako, pa mamariziro a mcerenje wa thamanda la pamtunda, ku khwalala la pa mwaniko wa wotsuka nsaru;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 7

Onani Yesaya 7:3 nkhani