6 Tiyeni, tikwere, timenyane ndi Yuda, timbvute; tiyeni, tidzigumulire mpata, pamenepo tikhazike mfumu pakati pace, ngakhale mwana wamwamuna wa Tabeeli;
Werengani mutu wathunthu Yesaya 7
Onani Yesaya 7:6 nkhani