Yesaya 10:13 BL92

13 Popeza anati, Mwa mphamvu ya dzanja langa ndacita ici, ndi mwa nzeru yanga; pakuti ine ndiri wocenjera; ndacotsa malekezero a anthu, ndalanda cuma cao, ndagwetsa monga munthu wolimba mtima iwo okhala pa mipando yacifumu;

Werengani mutu wathunthu Yesaya 10

Onani Yesaya 10:13 nkhani