Yesaya 10:20 BL92

20 Ndipo padzakhala tsiku lomwelo, kuti otsala a Israyeli, ndi iwo amene anapulumuka a nyumba ya Yakobo, sadzatsamiranso iye amene anawamenya; koma adzatsamira Yehova Woyera wa Israyeli, ntheradi.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 10

Onani Yesaya 10:20 nkhani