Yesaya 10:26 BL92

26 Ndipo Yehova wa makamu adzamuutsira cikoti, monga m'kuphedwa kwa Midyani pa thanthwe la Orebu; ndipo cibonga cace cidzakhala pamwamba pa nyanja, ndipo adzaisamula monga anacitira Aigupto,

Werengani mutu wathunthu Yesaya 10

Onani Yesaya 10:26 nkhani