Yesaya 10:3 BL92

3 Ndipo mudzacita ciani tsiku lakudza woyang'anira, ndi cipasuko cocokera kutari? mudzathawira kwa yani kufuna kuthangatidwa? mudzasiya kuti ulemerero wanu?

Werengani mutu wathunthu Yesaya 10

Onani Yesaya 10:3 nkhani