10 Cifukwa iwe waiwala Mulungu wa cipulumutso cako, sunakumbukira thanthwe la mphamvu zako; cifukwa cace iwe waoka mitengo yokondweretsa, waokapo zipinjiri zacilendo;
Werengani mutu wathunthu Yesaya 17
Onani Yesaya 17:10 nkhani