Yesaya 27:12 BL92

12 Ndipo padzakhala tsiku limenelo, kuti Yehova adzaomba tirigu wace, kucokera madzi a nyanja, kufikira ku mtsinje wa Aigupto, ndipo mudzakunkhidwa mmodzi, inu ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 27

Onani Yesaya 27:12 nkhani