Yesaya 29:7 BL92

7 Ndipo khamu la mitundu yonse yomenyana ndi Arieli, ngakhale yonse yomenyana naye ndi linga lace, ndi kumsautsa idzafanana ndi loto, masomphenya a usiku.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 29

Onani Yesaya 29:7 nkhani