Yesaya 38:5 BL92

5 Ukanene kwa Hezekiya, Atero Yehova, Mulungu wa Davide, kholo lako, Ndamva kupemphera kwako, ndaona misozi yako; taona, ndidzaonjezera pa masiku ako zaka khumi ndi zisanu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 38

Onani Yesaya 38:5 nkhani