Yesaya 40:31 BL92

31 koma iwo amene alindira Yehova adzatenganso mphamvu; adzauluka pamwamba ndi mapiko monga ziombankhanga; adzathamanga kuma osalema; adzayenda koma osalefuka.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 40

Onani Yesaya 40:31 nkhani