24 Iwe sunandigulire Ine nzimbe ndi ndarama, pena kundikhutitsa ndi mafuta a nsembe zako. Koma iwe wanditumikiritsa ndi macimo ako, wanditopetsa ndi mphulupulu zako.
Werengani mutu wathunthu Yesaya 43
Onani Yesaya 43:24 nkhani