Yesaya 49:25 BL92

25 Koma atero Yehova, Ngakhale am'nsinga a wamphamvu adzalandidwa, ndi cofunkha ca woopsya cidzapulumutsidwa; pakuti Ine ndidzakangana naye amene akangana ndi iwe, ndipo ndidzapulumutsa ana ako.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 49

Onani Yesaya 49:25 nkhani