Yesaya 5:20 BL92

20 Tsoka kwa iwo amene ayesa zoipa zabwino, ndi zabwino zoipa; amene aika mdima m'malo mwa kuyera, ndi kuyera m'malo mwa mdima; amene aika zowawa m'malo mwa zotsekemera, ndi zotsekemera m'malo mwa zowawa!

Werengani mutu wathunthu Yesaya 5

Onani Yesaya 5:20 nkhani