Yesaya 58:1 BL92

1 Pfuula zolimba, usalekerere, kweza mau ako ngati lipenga, ndi kuwafotokozera anthu anga colakwa cao, ndi banja la Yakobo macimo ao.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 58

Onani Yesaya 58:1 nkhani